TTB Chichewa cover art

All Episodes

TTB Chichewa — 261 episodes

#
Title
1

Ulamuliro Woipa Wa Manase

2

Kuchiritsidwa Kwa Hezekiya, Cholakwa Ndi Imfa Yake

3

Nkhawa Ya Hezekiya Ndi Ulosi Wa Yesaya

4

Chitsitsimutso Chikudza Ndi Hezekiya Ndipo Mulungu Ayesa Chikhulupiriro Cha A Yuda

5

Ahazi Akhala Mfumu Ya Yuda Pamene Israyeli Atengedwa Ukapolo

6

Ntchito Zomaliza Za Elisa; Mafumu Abwino Ndi Oipa A Israyeli

7

Yoasi Akhala Mfumu Ndi Ulamuliro Wake

8

Yehu Akhala Mfumu Ya Israyeli Ndi Chilango Pa Nyumba Ya Ahabu

9

Elisa Akwaniritsa Malonjezo Ake Ndi Chilango Kwa Oipa

10

Elisa Ayandamitsa Nkhwangwa Pa Madzi Ndi Chiwembu Cha Elisa Ku

11

Mbiri Ya Namaani Wa Ku Syria

12

Elisa Alowa M’malo Mwa Eliya Ndi

13

Moto Wa Kumwamba Woteteza Eliya Kwa Ahaziya Ndipo Eliya Akwera Kumwamba

14

Ahabu Ndi Munda Wa Naboti; Ahabu Ndi Mneneri Mikaya

15

Eliya Ali Pansi Pa Mtengo Wa Tsanya: Israyeli Amenyana Ndi Syria

16

Eliya Adzudzula Ahabu Ndipo Yehova Atsutsana Ndi Baala Pa Phiri La Kalimeri

17

Ukwati Wa Yezeberi Ndi Ahabu Ndi Kuti Eliya Alengeza Za Chilala Kwa Zaka Zitatu

18

Imfa Ya Rehabiamu Ndi Yerobiamu; Mafumu A Ufumu Wogawika

19

Chilango Pa Yerobiamu Ndi Yuda

20

Zinthu Zochititsa Manyazi Ndi Imfa Ya Solomoni; Kugawika Kwa Ufumu Pakati Pa Rehabiamu Ndi Yerobiamu

21

Ntchito Yomanga Kachisi Ndi Mwambo Wopereka Kachisi

22

Ntchito Yomanga Kachisi Ndi

23

Kukonzekera Ndi Kumanga Kachisi Wa Mulungu

24

Chopempha Cha Solomoni; Pemphero Lake Liyankhidwa Ndi Ukulu Wa Ufumu Wake

25

Upangiri Wa Davide Kwa Solomoni Ndipo Solomoni Apempha Nzeru

26

Kulephera Kwa Chiwembu Cha Adoniya; Solomoni Adzozedwa Mfumu; Malangizo A Davide Kwa Solomoni.

27

Mau Otsiriza A Davide; Anyamata A Davide Amphamvu Ndi Chiwerengero

28

Njala Mu Israyeli, Agibeoni Abwezera Nkhondo Ndi Afilisti

29

Davide Abwezeretsedwa Pa Ufumu Wake Ndipo Seeba Aukira

30

Nkhondo Pakati Pa Davide Ndi Absalomu

31

Abisalomu Aukira Atate Wake, Davide

32

Uchimo Wa Ana A Davide; Amoni Ndi Absalomo

33

Natani Adzudzula Davide Chifukwa Cha Uchimo Wake Ndipo Davide Alapa Chimolo

34

Davide Ayambana Ndi Ammoni Ndi Asuri Ndi Uchimo Uwiri Waukulu Wa Davide

35

Ufumu Wa Davide Ukhala Wamphamvu Ndipo Davide Akhala Pa Ubwezi Ndi Mefiboseti

36

Pangano La Mulungu Pa Kumanga Nyumba Ya Davide

37

Njira Zoyenera Ndi Zolakwika Zomwe Davide Anatenga Pobweretsa Likasa Ku Yerusalemu

38

Davide Akhazikitsidwa Mfumu Wa Israyeli Yense

39

Davide Akhazikitsidwa Mfumu

40

Sauli Ndi Jonatani Aphedwa Ku Nkhondo

41

Moyo Wa Davide Pamene Ali Pakati Pa Afilisti

42

Davide Abwerera Kudziko La Afilisti Pamene Sauli Apita Kwa Sing’anga

43

Davide Akwatira Abigayeli Ndipo Davide Asiya Kupha Sauli Kachiwiri

44

Chitetezo Ndi Chisamaliro Cha

45

Davide Asonkhanitsa Anyamata

46

Mulungu Alanga Davide; Ndipo Davide Apempha Ansembe Kuti Amuthandize

47

Mulungu Akuphunzitsa Davide; Sauli Afuna Kupha Davide; Ndipo Jonatani Amuthandiza Kuthawa

48

Davide Adzonzedwa Ndipo Akupha Goliati

49

Kusamvera Kwa Sauli Pa Agagi Ndipo Samueli Mudzudzula

50

Sauli Apandukira Mulungu; Yonatani Apambana Pankhondo Ya Afilisti; Komanso Kuipa Kwa Lamulo Lofulumira La Sauli

51

Sauli Agonjetsa Amoni Ndi Kuchoka Kwa Udindo Kwa Samueli Kupita Kwa Sauli

52

Sauli Asankhidwa Ndi Kudzozedwa

53

Chilango Cha Mulungu Pa Afilisti;

54

Kuitanidwa Kwa Samueli; Chilango Cha Mulungu Pa Eli Ndi Ana Ake Chikwanitsidwa; Komanso Chilango Cha Mulungu Pa Afilisti

55

Pemphero La Hana La Ulosi; Ana A Eli Woipa; Mwana Samueli M’kachis

56

Chiyambi Cha Bukhuli, Kubadwa Kwa Samueli

57

Chifundo Cha Anthu Akunja Machilitso Ya Yesu; Ulendo Wotsiriza Ku Roma Ndi Ayuda

58

Ulendo Wa Paulo Wamasautso Ukuptilira Panyanja Paoneka Mwera Ndi Kuonongeka Kwa Ngalawa

59

Paulo Atsika Ku Kaisareya Ndi Kuyamba Ulendo Wake Wa Pa Nyanja Wopita Ku Roma

60

Masautso A Paulo Akupitilira Pa Ulendo Wake Wa Ku Roma, Kuchitira Umboni Uitanidwa Ku Kaisareya

61

Ulendo Woopsa Wa Paulo Ukupitilira Ndi Umboni Ku Kaisareya

62

Ulendo Woopsa Wa Paulo Ku Roma Ukupitilira

63

Ulendo Woopsa Wa Paulo Ku Roma Ukupitirira

64

Zobvuta Zokonzedwa Ndi A Yuda Zikupitilira Pa Ulendo Wa Paulo Ku Aroma

65

Ulendo Wamasautso Wa Paulo Ku Roma

66

Maulendo A Paulo, Zochenjeza Kwa Paulo Ndi Kuti Akhala Ndi A Yuda

67

Utumiki Wa Paulo Ndi Umboni Wake Kwa Akulu Ku Efeso

68

Utumiki Wa Paulo Uchita Bwino Pa Zaka Ziwiri Mu Efeso; Gulu La Oukira Ndimlembi Abwino; Paulo Apita Ku Greece Ndi Ku Korinto

69

Paulo Ku Korinto Ndi Bvuto La Ayuda; Nthawi Pang’ono Ku Aefeso; Ulendo Wachitatu Wa Paulo

70

Paulo Alalikira Ku Atene Mkati

71

Uthenga Wabwino Ulandiridwa Ku Atesalonika Ndi Ku Berea; Ayuda

72

Paulo; Kuitanidwa Ku Ulaya Ndi Zochitika Ku Afilipi

73

Gawo La Chiwiri Loona Ngati M’dulidwe Ndi Lamulo La Mose Ndizofunika Kapena Ayi; Komanso Paulo Ndi Barnaba Apatukana

74

Gawo Loyamba La Loona Ngati Mdulidwe Ndi Lamulo La Mose Ndilofunika Kapena Ayi

75

Uthenga Wabwino Ulalikidwa Ku Ikoniyo, Lustra, Ndi Derbe; Kubwereranso Ku Lustra Ndi Ikoniyo Ndi Antiokeya; Ndi Kubwerera Kunyumba

76

Mulungu Aitana Barnaba Ndi Paulo; Zochitika Ku Kupro; Marko Abwerera Ndi Zochitika Ku Antiokeya

77

Petulo Atuluka Mndende, Paulo Ndi Banaba Abwelera Ku Antiyokeya

78

Mau A Petro Odziteteza Pophatikana Ndi Anthu A Amitundu Komanso Tiona Za Mpingo Wa Ku Antiokeya

79

Chipulumutso Cha A Amitundu Chikudza Ndi Mphamvu Ya Mulungu

80

Kutembenuka Mtima Kwa Saulo; Utumiki Wa Petro Ku Yopa Ndi Luda

81

Filipo Athandiza Mdindo Wa Ku Aitiopiya Kutembenuka Mtima

82

Masautso Akulu; Utumiki Wa Filipo; Chikhulupiriro Cha Simoni; Utumiki Wa Petro Ndi Yohane; Mlaliki Filipo

83

Kudzikanila Kwa Stefano Pamaso Pa Bwalo La Sanhedrin Ndi Imfa Yake

84

Udani Wa M’chikhalidwe; Kuyendetsa Mpingo Moopa Mulungu; Kukula Kwa Mpingo Muyerusalemu; Ndi Kuona Adani A Stefano

85

Kuchotsa Chodetsa Mumpingo; Kufalitsa Uthenga Kopambana Ndi Kuzunzika Kwa Mpingo Ndi Upangiri Wa Gamalieli

86

Kusakondwa Kwa Atsogoleri A Chiyuda Ndi Petro Ndi Yohane; Kuweruza Kwachilendo; Kuopseza;

87

Mphamvu za Mzimu Woyera, Petulo alalikiranso

88

Petulo ayankha otsutsana naye, Uneneri wa Yoeli; Petulo alalika Yesu anthu 3,000 nkutembenuka mtima

89

Kuyamba kwa mpingo komanso ubatizo wa Mzimu Woyera

90

Yesu alangiza Ophunzira ake, alonjeza mzimu woyera komanso za kukwera kwake

91

Mlatho komanso Mbiri ya bukhu

92

Rute mumtima komanso pakhomo la Boazi

93

Rute asankha Boazi ngati mlowamalo

94

Rute kukunkha kwa Boazi

95

Rute Apitiliza Kukunkha Chakudya M’munda Wa Boazi

96

Rute Akunkha Chakudya M’munda Wa Boazi

97

Kubwerera ku Betelehemu

98

Chiyambi, Kulowa ku Moabu

99

Dziko lilowerera pauzimu ndi pa ndale

100

Oweruza Samusoni

101

Nsanje ya Efurayimu, za oweruza ena anatu

102

Yefuta abweretsa chipambano kwa Amoni

103

Utsogoleri wakanika

104

Zaka 40 zamtendere pansi pa utsogoleri wa Gidiyoni

105

Mulungu apulumutsa Israyeli kudzera mwa Gidiyoni

106

Kulowelera kwa kachisanu ndi chimodzi

107

Nyimbo ya Debora ndi Baraki

108

Mulungu agwiritsa anthu wamba kupulumutsa Israyeli

109

Zochitika ku Israyeli atamwalira Yoshua

110

Uthenga womaliza wa Yoshuwa

111

Midzi Ya A Levi Ndi Midzi Iwiri Ya Hafu Ikhala Kum’mawa Kwa Yordano

112

Kumaliza Kugawa Madera Kwa Ana A Israyeli Ndi Midzi Yopulumukiramo

113

Kudula Malire A Malo A Mapfuko Ya Ana A Israyeli

114

Dziko La Kum’mawa Kwa Mtsinje Wa Yordano Ndi Gawo La Kalebe

115

Kutsiriza Nkhondo Ya Kum’mwera Ndi Kupita Kumpoto Kwa Kanani

116

A Gibeoni Ndi Nkhondo Yochokera Kum’mwera

117

Israyeli Alephera kugonjetsa Ai Kenaka Tiona Kupasuka kwake

118

Kugonjetsa Mudzi Wa Yeriko

119

Zinthu Zitatu Zochitika Komanso Zofunika Kwambiri

120

Israyeli Aoloka Mtsinje Wa Yordano

121

Yoswa Atenga Ulamuliro Pa Israyeli

122

Chiyambi Cha Bukhu La Yoswa, Yoswa Atenga Udindo Ndi

123

Nyimbo Ya Mose, Mdalitso Ndi Imfa Yake Ulamuliro Wake

124

Moyo Ndi Zabwino Kulinganiza Ndi Imfa Ndi Zoyipa; Kusintha Kwa Utsogoleri

125

Pangano La Dziko La Malonjezano

126

Malonjezo A Mulungu; Madalitso Pakumvera Ndi Tsoka Pa kusamvera

127

Kukwapula Wolakwa, Kuteteza Mkazi Wamasiye, Chilango Cha Amaleke, Ndi Chopereka Cha Zipatso Zoyamba

128

Kukhala Mu Israyeli, Ukhondo, Malamulo A Mose Pa Kuthetsa Ukwati Ndi Malamulo Wena

129

Chilango Chopachikidwa Pamtengo; Za

130

Malamulo A Nkhondo, Kupha, Amayi

131

Mesiya, Mneneri Woona Ndi Onama, Midzi Yopulumikira Ndi Malamulo Wena

132

Kumtumikira Mulungu Ndi Mtima Wonse;

133

Chaka Chopuma, Ukapolo, Madyerero Atatu, Kuweruza Ndi Kupembedza Mafano

134

Kupitiliza Za Aneneri Onama; Midzi Yonyasa; Chikhalidwe Ndi malamulo apa Chakudya ndi chakhumi

135

Lamulo Lakutenga Malo, Malo Amodzi Opembedzerapo, Malamulo A Zakudya Ndi Kuchenjeza Za Aneneri Onama

136

Kulephera Kwa Israyeli; Miyala Ya Malamulo Atsopano; Kupembedzera Kwa Mose; Kupatulidwa Kwa A Levi; Chisamaliro Cha Mulungu; Ndi Lamulo La Kutenga Malo

137

Zomwe Anachita Mulungu M’mbuyomo, Ndizimene Zimapereka Chilimbikitso Pa Zomwe Mulungu Adzachite

138

Chipulumutso Ndiubale Omwe

139

Mose Apereka Ndi Kumasuliranso Malamulo

140

Chikondi Cha Mulungu Chionekera Mwa Isarayeli Ndipo Ayenera Kuphunzitsa Ana Kupembedza Mulungu M’mzimu

141

Mose Aunikanso Za Kulephera Kwa Israyeli M’njira Zosiyana-Siyana Ndipo awalimbikitsa Kuti Amvere Mulungu

142

Chiyambi Cha Bukhu La Deuterenomo Ndi Kuona Za Uchimo WaIsrayeli Pa Kadesi Barnea

143

Mau Omaliza A Yohane Otseka Nawo Bukhu

144

Ophunzira Aona Yesu Atauka Kumanda

145

Kuuka Ku Manda Kwa Yesu Kristu

146

Imfa Ya Yesu Pa Mtanda

147

Yesu Kubwalo La Annasi Ndi Pilato

148

Yesu Agwidwa M’munda Wa Getsemane

149

Yesu Apempherera Ophunzira Wake M’nyengo Yonse

150

Yesu Apenya Mtsogolo Ndi Chiyembekezo Cha Mtanda

151

Kupitiliza Kuphunzitsa Za Mzimu Woyera

152

Yesu Achenjeza Za Kubwera Kwa Otsutsa

153

Wophunzira Ayenera Kukhala Mwa Yesu Ndi Kumumvera Iye

154

Yesu Adzitchula Kukhala Mpesa Ndipo Ophunzira Ake Ndiwo Nthambi

155

Yesu Alonjeza Mzimu Woyera

156

Yesu Alimbikitsa Ophunzira Wake

157

Yudase Achoka Ndipo Yesu Aneneratu Kuti Petro Adzamukana Iye

158

Yesu Asambitsa Mapazi Ya Ophunzira Ake

159

Yesu Alowa M’nthawi Ya Masautso

160

M’yuda Ndi Ahelene Achitira Yesu Umboni

161

Yesu Aukitsa Lazaro Kwa Akufa

162

Yesu Akonzekeretsa Ophunzira Wake Kuti Akumane Ndi Lazaro

163

Yesu Akudziula Kuti Ndiye M’busa Wabwino

164

Israyeli Akuonetsa Chithunzi Chakuti Ndikhola La Nkhosa

165

Munthu Wosaona Uja, Tsopano Waona Yesu

166

Yesu Atsegula Maso A Munthu Amene Anabadwa Ali Wakhungu

167

Yesu Akudziulura Kuti Ndiye Kuunika Kwa Dziko Lapansi

168

Yesu Akhulukira Mkazi Wogwidwa Chigololo

169

Udani Ukukula Pa Yesu

170

Yesu Apitiliza Kuphunzitsa Za Mkate Wamoyo

171

Yesu Adziulula Kuti Ndiye Mkate Wa moyo

172

Yesu Adyetsa Anthu Zikwi Zisanu (5,000) Komanso Ayenda Pa Nyanja

173

Yesu Atsimikiza Kunena Kuti Iye Ndi Atate Wake, Ali Amodzi

174

Yesu Aulura Umulungu Wake Ndipo Ayuda Atsutsana Naye

175

Chipulumutso M’mudzi Wa Samariya

176

Yesu Akumana Ndi Mkazi Pa Chitsime

177

Ulendo Wa Nikodemo Ndi Umboni Wa Yohane M’batizi

178

Yesu Agwiritsa Ntchito Mau Poyeretsa Kachisi Ndi Nkhani Ya Nikodemo

179

Ntchito Yoyamba Ya Yesu Pa Ukwati Wa Ku Kana

180

Umboni Wochitira Yesu Wa Anthu Anayi

181

Umunthu Wa Mwana Wa Mulungu

182

Mau Auuluridwa /Afotokonzeredwa

183

Chilango Cha Amidyani, Rubeni Ndi Gadi Afuna Dziko Lawo, lamulo La Kutenga Dziko, Malire A Dziko Lamalonjezano, Midzi Ya Alevi Ndi Lamulo Lacholowa

184

Kupitiliza Kuona Za Lamulo La Kaperekedwe Ka Nsembe, Ndi Malumbiro

185

Cholowa Cha Wana Wa Akazi, Mose Akonzekera Kufa, Zopereka Ndi Kulambira Koona

186

Ulosi Wachinayi, Nzeru Ya Balamu Ndi Chiwerengero Cha M’badwo Watsopano

187

Balaki Afuna Baalamu Kuti Atemberere Israyeli, Koma Baalamu Adalitsa Israyeli

188

Chigonjetso Cha A Israyeli, Kudandaula Kwa Chisanu Ndi Chitatu, Njoka Ya Mkuwa, Nyimbo Yachiyamiko Ndi Za Balak Ndi Balaamu

189

Kudandaula Pa Kadeshi, Madzi Aturuka

190

Aroni Ndi Alevi Akhazikitsidwa Pa Ntchito Yawo, Ndi Kuunika Udindo Wawo

191

Kuukira Kwa Kukulu Ndikutsatira Chilango Chachikulu, Komanso Kuukanso Kwa Aroni

192

Kuunikanso Kuti Chikonzero Cha Yehova Sichidaonongeke, Chilango Cha Imfa Posasunga Sabata, Kuukira Kwa Kora

193

Mose Atuma Akazonde, Israyeli Sakukhulupilira Mulungu, Chilango Cha Mulungu Ndi Kulapa Kwa Israyeli

194

Mana, Mose Adandaula, Mulungu

195

Malipenga A Siliver, Mpongozi Wa Mose Ndipo A Israyeli Ayamba Kuyenda Ndipo Adandaula

196

Kuwala Kuchokera Kuchoyikapo Nyali, Alevi Ayeretsedwa, Paskha Ndi Kutsogoleredwa Kwa Israyeli

197

Kufunika Kwa Lumbiro La Unanziri Ndi Madalitso Autatu Wa Mulungu Ndi mphatso zake

198

Kudetsedwa Kudzera Mwa Nthenda Ndi Uchimo

199

Pfuko La Alevi Pamodzi Ndi Ntchito Yawo, Lipatsidwa Kwa Wansembe Wamkulu

200

Mtsitsi Kapena Muzu Wa Ana A Israyeli Ndi Kakhalidwe Kadongosolo Ka Pa Chigono

201

Chiyambi Cha Bukhu Ndi Kuwerengedwa Kwa Ana A Israyeli

202

Yesu Adziwonetsa Kwa Anthu Ambiri Ndi Kukwera Kumwamba

203

Yesu Ayikidwa M’manda Ndi Kuuka Kwa Akufa

204

Yesu Achoka Kubwalo La Milandu Kupita Kukapachikidwa

205

Amgwira Yesu Ndipo Apita Naye Kumabwalo Ya Mirandu

206

Zochitika Zomwe Zikuonetsa Kumalizika Kwa Utumiki Wa Yesu

207

Yesu Ayankha Funso Lakuti Kodi Zinthu Izi Zidzaoneka Liti?

208

Yesu Akufunsidwa Za Ulamuliro Wake Ndipo Yesu Akuwayankha

209

Yesu Alirira Mzinda Wa Yerusalemu

210

Yesu Aphunzitsa Kupyolera M’mafanizo Osiyana Siyana Komanso Adalitsa Wana

211

Yesu Alangiza Wophunzira Onse

212

Fanizo La Kapitawo Wonyenga Ndi Yankho La Yesu Kwa Afarisi

213

Yesu Akuphunzitsa Kudzera M’mafanizo A Nkhosa Yosokera, Ndalama Yotayika, Ndi Wana Awiri Wolowerera

214

Yesu Aphunzitsa Kudzera M’mafanizo Osiyana-Siyana

215

Yesu Akupitiliza Kuphunzitsa Ndi Kuchilitsa Pa Ulendo Waku Yerusalemu

216

Yesu Aphunzitsa Ndi Mafanizo Ambiri

217

Yesu Aphunzitsa Za Pemphero Komanso Adzudzula Afarisi

218

Fanizo La Msamariya Wachifundo

219

Ulendo Wa Yesu Ku Yerusalemu

220

Yesu Aphunzitsa Kudzera M’mafanizo

221

Machilitso, Kuukitsa Akufa Ndi Kuyamikira Yohane M’batizi

222

Kusankha Ophunzira Khumi Ndi Awiri Ndi Chiphunzitso Chapachigwa

223

Yesu Asankha Ophunzira, Achiritsa Ndi Kuphunzitsa

224

Yesu Akanidwa Ndi Abale Wake

225

Yohane M’batizi; Kuunika Muzu WaMariya, Komanso Kuyesedwa Kwa Yesu

226

Simeoni Ndi Anna Azindikira Mesiya; M’nyamata Yesu Ali M’kachisi; Kuyambika Kwa Utumiki Wa Yohane

227

Zinthu Zomwe Zinachitika Kwa Mariya

228

Nyimbo Za Khisimisi

229

Kulengeza Kwa M’ngelo Gabrieli

230

Chiyambi Ndi Kuonetsa Cholinga Cha Bukhuli

231

Kugwiritsa Ntchito Pangano

232

Tsogolo La Mtundu Wa Israyeli

233

Chaka Chopuma Ndi Chaka Chachikondwerero

234

Choyikapo Nyali Ndi Mkate Woonekera

235

Kupitiliza Kuona Za Nyengo Yopatulika

236

Nyengo Kapena Nthawi Yopatulika

237

Kudetsedwa Kwa Unsembe Ndi Maliro

238

Chilango Cha Kupha

239

Ubale Wa Munthu

240

Makhalidwe Oyenera Ya Ana Amulungu

241

Pali Malo Amodzi Operekera Nsembe

242

Tsiku Lotetezera

243

Kuunika Zo Ukha

244

Mabala Akukha Kapena Mabala Otuluka Magazi

245

Mwambo Woyeretsa Munthu Wakhate

246

Kupitiliza Kuona Nkhani Ya Khate

247

Tikambirana Za Nthenda Ya Khate

248

Kutengera Uchimo Kuchokera Kwa Makolo Kapena Kuti Kupatsirana Machimo Kuchokera Kwa Makolo

249

Nyama Zodetsedwa Ndi Zosadetsedwa

250

Chakudya Cha Anthu A Mulungu

251

Mulungu Athana Ndi Kugalukira Ndi Kusamvera

252

Ntchito Ya Tsiku Ndi Tsiku Ya Ansembe

253

Kupatulika Kwa Ansembe

254

Nsembe Yopalamula Ndi Nsembe Ya Mtendere

255

Kuunika Za Nsembe Yopalamula

256

Zochimwa Za Mtundu Wonse Wa Israyeli, Mtsogoleri Ndi Anthu Wamba

257

Nsembe Ya Uchimo Pochimwa Wansembe

258

Nsembe Ya Mtendere

259

Nsembe Ya Ufa Ndi Ya Zipatso Zoyamba

260

Malamulo, Mwambo Ndi Chifukwa Chopereka Yopsereza

261

Chiyambi Cha Bukhu La Levitiko Ndi Za Nsembe Yopsereza