All Episodes
TTB Chichewa — 261 episodes
Ulamuliro Woipa Wa Manase
Kuchiritsidwa Kwa Hezekiya, Cholakwa Ndi Imfa Yake
Nkhawa Ya Hezekiya Ndi Ulosi Wa Yesaya
Chitsitsimutso Chikudza Ndi Hezekiya Ndipo Mulungu Ayesa Chikhulupiriro Cha A Yuda
Ahazi Akhala Mfumu Ya Yuda Pamene Israyeli Atengedwa Ukapolo
Ntchito Zomaliza Za Elisa; Mafumu Abwino Ndi Oipa A Israyeli
Yoasi Akhala Mfumu Ndi Ulamuliro Wake
Yehu Akhala Mfumu Ya Israyeli Ndi Chilango Pa Nyumba Ya Ahabu
Elisa Akwaniritsa Malonjezo Ake Ndi Chilango Kwa Oipa
Elisa Ayandamitsa Nkhwangwa Pa Madzi Ndi Chiwembu Cha Elisa Ku
Mbiri Ya Namaani Wa Ku Syria
Elisa Alowa M’malo Mwa Eliya Ndi
Moto Wa Kumwamba Woteteza Eliya Kwa Ahaziya Ndipo Eliya Akwera Kumwamba
Ahabu Ndi Munda Wa Naboti; Ahabu Ndi Mneneri Mikaya
Eliya Ali Pansi Pa Mtengo Wa Tsanya: Israyeli Amenyana Ndi Syria
Eliya Adzudzula Ahabu Ndipo Yehova Atsutsana Ndi Baala Pa Phiri La Kalimeri
Ukwati Wa Yezeberi Ndi Ahabu Ndi Kuti Eliya Alengeza Za Chilala Kwa Zaka Zitatu
Imfa Ya Rehabiamu Ndi Yerobiamu; Mafumu A Ufumu Wogawika
Chilango Pa Yerobiamu Ndi Yuda
Zinthu Zochititsa Manyazi Ndi Imfa Ya Solomoni; Kugawika Kwa Ufumu Pakati Pa Rehabiamu Ndi Yerobiamu
Ntchito Yomanga Kachisi Ndi Mwambo Wopereka Kachisi
Ntchito Yomanga Kachisi Ndi
Kukonzekera Ndi Kumanga Kachisi Wa Mulungu
Chopempha Cha Solomoni; Pemphero Lake Liyankhidwa Ndi Ukulu Wa Ufumu Wake
Upangiri Wa Davide Kwa Solomoni Ndipo Solomoni Apempha Nzeru
Kulephera Kwa Chiwembu Cha Adoniya; Solomoni Adzozedwa Mfumu; Malangizo A Davide Kwa Solomoni.
Mau Otsiriza A Davide; Anyamata A Davide Amphamvu Ndi Chiwerengero
Njala Mu Israyeli, Agibeoni Abwezera Nkhondo Ndi Afilisti
Davide Abwezeretsedwa Pa Ufumu Wake Ndipo Seeba Aukira
Nkhondo Pakati Pa Davide Ndi Absalomu
Abisalomu Aukira Atate Wake, Davide
Uchimo Wa Ana A Davide; Amoni Ndi Absalomo
Natani Adzudzula Davide Chifukwa Cha Uchimo Wake Ndipo Davide Alapa Chimolo
Davide Ayambana Ndi Ammoni Ndi Asuri Ndi Uchimo Uwiri Waukulu Wa Davide
Ufumu Wa Davide Ukhala Wamphamvu Ndipo Davide Akhala Pa Ubwezi Ndi Mefiboseti
Pangano La Mulungu Pa Kumanga Nyumba Ya Davide
Njira Zoyenera Ndi Zolakwika Zomwe Davide Anatenga Pobweretsa Likasa Ku Yerusalemu
Davide Akhazikitsidwa Mfumu Wa Israyeli Yense
Davide Akhazikitsidwa Mfumu
Sauli Ndi Jonatani Aphedwa Ku Nkhondo
Moyo Wa Davide Pamene Ali Pakati Pa Afilisti
Davide Abwerera Kudziko La Afilisti Pamene Sauli Apita Kwa Sing’anga
Davide Akwatira Abigayeli Ndipo Davide Asiya Kupha Sauli Kachiwiri
Chitetezo Ndi Chisamaliro Cha
Davide Asonkhanitsa Anyamata
Mulungu Alanga Davide; Ndipo Davide Apempha Ansembe Kuti Amuthandize
Mulungu Akuphunzitsa Davide; Sauli Afuna Kupha Davide; Ndipo Jonatani Amuthandiza Kuthawa
Davide Adzonzedwa Ndipo Akupha Goliati
Kusamvera Kwa Sauli Pa Agagi Ndipo Samueli Mudzudzula
Sauli Apandukira Mulungu; Yonatani Apambana Pankhondo Ya Afilisti; Komanso Kuipa Kwa Lamulo Lofulumira La Sauli
Sauli Agonjetsa Amoni Ndi Kuchoka Kwa Udindo Kwa Samueli Kupita Kwa Sauli
Sauli Asankhidwa Ndi Kudzozedwa
Chilango Cha Mulungu Pa Afilisti;
Kuitanidwa Kwa Samueli; Chilango Cha Mulungu Pa Eli Ndi Ana Ake Chikwanitsidwa; Komanso Chilango Cha Mulungu Pa Afilisti
Pemphero La Hana La Ulosi; Ana A Eli Woipa; Mwana Samueli M’kachis
Chiyambi Cha Bukhuli, Kubadwa Kwa Samueli
Chifundo Cha Anthu Akunja Machilitso Ya Yesu; Ulendo Wotsiriza Ku Roma Ndi Ayuda
Ulendo Wa Paulo Wamasautso Ukuptilira Panyanja Paoneka Mwera Ndi Kuonongeka Kwa Ngalawa
Paulo Atsika Ku Kaisareya Ndi Kuyamba Ulendo Wake Wa Pa Nyanja Wopita Ku Roma
Masautso A Paulo Akupitilira Pa Ulendo Wake Wa Ku Roma, Kuchitira Umboni Uitanidwa Ku Kaisareya
Ulendo Woopsa Wa Paulo Ukupitilira Ndi Umboni Ku Kaisareya
Ulendo Woopsa Wa Paulo Ku Roma Ukupitilira
Ulendo Woopsa Wa Paulo Ku Roma Ukupitirira
Zobvuta Zokonzedwa Ndi A Yuda Zikupitilira Pa Ulendo Wa Paulo Ku Aroma
Ulendo Wamasautso Wa Paulo Ku Roma
Maulendo A Paulo, Zochenjeza Kwa Paulo Ndi Kuti Akhala Ndi A Yuda
Utumiki Wa Paulo Ndi Umboni Wake Kwa Akulu Ku Efeso
Utumiki Wa Paulo Uchita Bwino Pa Zaka Ziwiri Mu Efeso; Gulu La Oukira Ndimlembi Abwino; Paulo Apita Ku Greece Ndi Ku Korinto
Paulo Ku Korinto Ndi Bvuto La Ayuda; Nthawi Pang’ono Ku Aefeso; Ulendo Wachitatu Wa Paulo
Paulo Alalikira Ku Atene Mkati
Uthenga Wabwino Ulandiridwa Ku Atesalonika Ndi Ku Berea; Ayuda
Paulo; Kuitanidwa Ku Ulaya Ndi Zochitika Ku Afilipi
Gawo La Chiwiri Loona Ngati M’dulidwe Ndi Lamulo La Mose Ndizofunika Kapena Ayi; Komanso Paulo Ndi Barnaba Apatukana
Gawo Loyamba La Loona Ngati Mdulidwe Ndi Lamulo La Mose Ndilofunika Kapena Ayi
Uthenga Wabwino Ulalikidwa Ku Ikoniyo, Lustra, Ndi Derbe; Kubwereranso Ku Lustra Ndi Ikoniyo Ndi Antiokeya; Ndi Kubwerera Kunyumba
Mulungu Aitana Barnaba Ndi Paulo; Zochitika Ku Kupro; Marko Abwerera Ndi Zochitika Ku Antiokeya
Petulo Atuluka Mndende, Paulo Ndi Banaba Abwelera Ku Antiyokeya
Mau A Petro Odziteteza Pophatikana Ndi Anthu A Amitundu Komanso Tiona Za Mpingo Wa Ku Antiokeya
Chipulumutso Cha A Amitundu Chikudza Ndi Mphamvu Ya Mulungu
Kutembenuka Mtima Kwa Saulo; Utumiki Wa Petro Ku Yopa Ndi Luda
Filipo Athandiza Mdindo Wa Ku Aitiopiya Kutembenuka Mtima
Masautso Akulu; Utumiki Wa Filipo; Chikhulupiriro Cha Simoni; Utumiki Wa Petro Ndi Yohane; Mlaliki Filipo
Kudzikanila Kwa Stefano Pamaso Pa Bwalo La Sanhedrin Ndi Imfa Yake
Udani Wa M’chikhalidwe; Kuyendetsa Mpingo Moopa Mulungu; Kukula Kwa Mpingo Muyerusalemu; Ndi Kuona Adani A Stefano
Kuchotsa Chodetsa Mumpingo; Kufalitsa Uthenga Kopambana Ndi Kuzunzika Kwa Mpingo Ndi Upangiri Wa Gamalieli
Kusakondwa Kwa Atsogoleri A Chiyuda Ndi Petro Ndi Yohane; Kuweruza Kwachilendo; Kuopseza;
Mphamvu za Mzimu Woyera, Petulo alalikiranso
Petulo ayankha otsutsana naye, Uneneri wa Yoeli; Petulo alalika Yesu anthu 3,000 nkutembenuka mtima
Kuyamba kwa mpingo komanso ubatizo wa Mzimu Woyera
Yesu alangiza Ophunzira ake, alonjeza mzimu woyera komanso za kukwera kwake
Mlatho komanso Mbiri ya bukhu
Rute mumtima komanso pakhomo la Boazi
Rute asankha Boazi ngati mlowamalo
Rute kukunkha kwa Boazi
Rute Apitiliza Kukunkha Chakudya M’munda Wa Boazi
Rute Akunkha Chakudya M’munda Wa Boazi
Kubwerera ku Betelehemu
Chiyambi, Kulowa ku Moabu
Dziko lilowerera pauzimu ndi pa ndale
Oweruza Samusoni
Nsanje ya Efurayimu, za oweruza ena anatu
Yefuta abweretsa chipambano kwa Amoni
Utsogoleri wakanika
Zaka 40 zamtendere pansi pa utsogoleri wa Gidiyoni
Mulungu apulumutsa Israyeli kudzera mwa Gidiyoni
Kulowelera kwa kachisanu ndi chimodzi
Nyimbo ya Debora ndi Baraki
Mulungu agwiritsa anthu wamba kupulumutsa Israyeli
Zochitika ku Israyeli atamwalira Yoshua
Uthenga womaliza wa Yoshuwa
Midzi Ya A Levi Ndi Midzi Iwiri Ya Hafu Ikhala Kum’mawa Kwa Yordano
Kumaliza Kugawa Madera Kwa Ana A Israyeli Ndi Midzi Yopulumukiramo
Kudula Malire A Malo A Mapfuko Ya Ana A Israyeli
Dziko La Kum’mawa Kwa Mtsinje Wa Yordano Ndi Gawo La Kalebe
Kutsiriza Nkhondo Ya Kum’mwera Ndi Kupita Kumpoto Kwa Kanani
A Gibeoni Ndi Nkhondo Yochokera Kum’mwera
Israyeli Alephera kugonjetsa Ai Kenaka Tiona Kupasuka kwake
Kugonjetsa Mudzi Wa Yeriko
Zinthu Zitatu Zochitika Komanso Zofunika Kwambiri
Israyeli Aoloka Mtsinje Wa Yordano
Yoswa Atenga Ulamuliro Pa Israyeli
Chiyambi Cha Bukhu La Yoswa, Yoswa Atenga Udindo Ndi
Nyimbo Ya Mose, Mdalitso Ndi Imfa Yake Ulamuliro Wake
Moyo Ndi Zabwino Kulinganiza Ndi Imfa Ndi Zoyipa; Kusintha Kwa Utsogoleri
Pangano La Dziko La Malonjezano
Malonjezo A Mulungu; Madalitso Pakumvera Ndi Tsoka Pa kusamvera
Kukwapula Wolakwa, Kuteteza Mkazi Wamasiye, Chilango Cha Amaleke, Ndi Chopereka Cha Zipatso Zoyamba
Kukhala Mu Israyeli, Ukhondo, Malamulo A Mose Pa Kuthetsa Ukwati Ndi Malamulo Wena
Chilango Chopachikidwa Pamtengo; Za
Malamulo A Nkhondo, Kupha, Amayi
Mesiya, Mneneri Woona Ndi Onama, Midzi Yopulumikira Ndi Malamulo Wena
Kumtumikira Mulungu Ndi Mtima Wonse;
Chaka Chopuma, Ukapolo, Madyerero Atatu, Kuweruza Ndi Kupembedza Mafano
Kupitiliza Za Aneneri Onama; Midzi Yonyasa; Chikhalidwe Ndi malamulo apa Chakudya ndi chakhumi
Lamulo Lakutenga Malo, Malo Amodzi Opembedzerapo, Malamulo A Zakudya Ndi Kuchenjeza Za Aneneri Onama
Kulephera Kwa Israyeli; Miyala Ya Malamulo Atsopano; Kupembedzera Kwa Mose; Kupatulidwa Kwa A Levi; Chisamaliro Cha Mulungu; Ndi Lamulo La Kutenga Malo
Zomwe Anachita Mulungu M’mbuyomo, Ndizimene Zimapereka Chilimbikitso Pa Zomwe Mulungu Adzachite
Chipulumutso Ndiubale Omwe
Mose Apereka Ndi Kumasuliranso Malamulo
Chikondi Cha Mulungu Chionekera Mwa Isarayeli Ndipo Ayenera Kuphunzitsa Ana Kupembedza Mulungu M’mzimu
Mose Aunikanso Za Kulephera Kwa Israyeli M’njira Zosiyana-Siyana Ndipo awalimbikitsa Kuti Amvere Mulungu
Chiyambi Cha Bukhu La Deuterenomo Ndi Kuona Za Uchimo WaIsrayeli Pa Kadesi Barnea
Mau Omaliza A Yohane Otseka Nawo Bukhu
Ophunzira Aona Yesu Atauka Kumanda
Kuuka Ku Manda Kwa Yesu Kristu
Imfa Ya Yesu Pa Mtanda
Yesu Kubwalo La Annasi Ndi Pilato
Yesu Agwidwa M’munda Wa Getsemane
Yesu Apempherera Ophunzira Wake M’nyengo Yonse
Yesu Apenya Mtsogolo Ndi Chiyembekezo Cha Mtanda
Kupitiliza Kuphunzitsa Za Mzimu Woyera
Yesu Achenjeza Za Kubwera Kwa Otsutsa
Wophunzira Ayenera Kukhala Mwa Yesu Ndi Kumumvera Iye
Yesu Adzitchula Kukhala Mpesa Ndipo Ophunzira Ake Ndiwo Nthambi
Yesu Alonjeza Mzimu Woyera
Yesu Alimbikitsa Ophunzira Wake
Yudase Achoka Ndipo Yesu Aneneratu Kuti Petro Adzamukana Iye
Yesu Asambitsa Mapazi Ya Ophunzira Ake
Yesu Alowa M’nthawi Ya Masautso
M’yuda Ndi Ahelene Achitira Yesu Umboni
Yesu Aukitsa Lazaro Kwa Akufa
Yesu Akonzekeretsa Ophunzira Wake Kuti Akumane Ndi Lazaro
Yesu Akudziula Kuti Ndiye M’busa Wabwino
Israyeli Akuonetsa Chithunzi Chakuti Ndikhola La Nkhosa
Munthu Wosaona Uja, Tsopano Waona Yesu
Yesu Atsegula Maso A Munthu Amene Anabadwa Ali Wakhungu
Yesu Akudziulura Kuti Ndiye Kuunika Kwa Dziko Lapansi
Yesu Akhulukira Mkazi Wogwidwa Chigololo
Udani Ukukula Pa Yesu
Yesu Apitiliza Kuphunzitsa Za Mkate Wamoyo
Yesu Adziulula Kuti Ndiye Mkate Wa moyo
Yesu Adyetsa Anthu Zikwi Zisanu (5,000) Komanso Ayenda Pa Nyanja
Yesu Atsimikiza Kunena Kuti Iye Ndi Atate Wake, Ali Amodzi
Yesu Aulura Umulungu Wake Ndipo Ayuda Atsutsana Naye
Chipulumutso M’mudzi Wa Samariya
Yesu Akumana Ndi Mkazi Pa Chitsime
Ulendo Wa Nikodemo Ndi Umboni Wa Yohane M’batizi
Yesu Agwiritsa Ntchito Mau Poyeretsa Kachisi Ndi Nkhani Ya Nikodemo
Ntchito Yoyamba Ya Yesu Pa Ukwati Wa Ku Kana
Umboni Wochitira Yesu Wa Anthu Anayi
Umunthu Wa Mwana Wa Mulungu
Mau Auuluridwa /Afotokonzeredwa
Chilango Cha Amidyani, Rubeni Ndi Gadi Afuna Dziko Lawo, lamulo La Kutenga Dziko, Malire A Dziko Lamalonjezano, Midzi Ya Alevi Ndi Lamulo Lacholowa
Kupitiliza Kuona Za Lamulo La Kaperekedwe Ka Nsembe, Ndi Malumbiro
Cholowa Cha Wana Wa Akazi, Mose Akonzekera Kufa, Zopereka Ndi Kulambira Koona
Ulosi Wachinayi, Nzeru Ya Balamu Ndi Chiwerengero Cha M’badwo Watsopano
Balaki Afuna Baalamu Kuti Atemberere Israyeli, Koma Baalamu Adalitsa Israyeli
Chigonjetso Cha A Israyeli, Kudandaula Kwa Chisanu Ndi Chitatu, Njoka Ya Mkuwa, Nyimbo Yachiyamiko Ndi Za Balak Ndi Balaamu
Kudandaula Pa Kadeshi, Madzi Aturuka
Aroni Ndi Alevi Akhazikitsidwa Pa Ntchito Yawo, Ndi Kuunika Udindo Wawo
Kuukira Kwa Kukulu Ndikutsatira Chilango Chachikulu, Komanso Kuukanso Kwa Aroni
Kuunikanso Kuti Chikonzero Cha Yehova Sichidaonongeke, Chilango Cha Imfa Posasunga Sabata, Kuukira Kwa Kora
Mose Atuma Akazonde, Israyeli Sakukhulupilira Mulungu, Chilango Cha Mulungu Ndi Kulapa Kwa Israyeli
Mana, Mose Adandaula, Mulungu
Malipenga A Siliver, Mpongozi Wa Mose Ndipo A Israyeli Ayamba Kuyenda Ndipo Adandaula
Kuwala Kuchokera Kuchoyikapo Nyali, Alevi Ayeretsedwa, Paskha Ndi Kutsogoleredwa Kwa Israyeli
Kufunika Kwa Lumbiro La Unanziri Ndi Madalitso Autatu Wa Mulungu Ndi mphatso zake
Kudetsedwa Kudzera Mwa Nthenda Ndi Uchimo
Pfuko La Alevi Pamodzi Ndi Ntchito Yawo, Lipatsidwa Kwa Wansembe Wamkulu
Mtsitsi Kapena Muzu Wa Ana A Israyeli Ndi Kakhalidwe Kadongosolo Ka Pa Chigono
Chiyambi Cha Bukhu Ndi Kuwerengedwa Kwa Ana A Israyeli
Yesu Adziwonetsa Kwa Anthu Ambiri Ndi Kukwera Kumwamba
Yesu Ayikidwa M’manda Ndi Kuuka Kwa Akufa
Yesu Achoka Kubwalo La Milandu Kupita Kukapachikidwa
Amgwira Yesu Ndipo Apita Naye Kumabwalo Ya Mirandu
Zochitika Zomwe Zikuonetsa Kumalizika Kwa Utumiki Wa Yesu
Yesu Ayankha Funso Lakuti Kodi Zinthu Izi Zidzaoneka Liti?
Yesu Akufunsidwa Za Ulamuliro Wake Ndipo Yesu Akuwayankha
Yesu Alirira Mzinda Wa Yerusalemu
Yesu Aphunzitsa Kupyolera M’mafanizo Osiyana Siyana Komanso Adalitsa Wana
Yesu Alangiza Wophunzira Onse
Fanizo La Kapitawo Wonyenga Ndi Yankho La Yesu Kwa Afarisi
Yesu Akuphunzitsa Kudzera M’mafanizo A Nkhosa Yosokera, Ndalama Yotayika, Ndi Wana Awiri Wolowerera
Yesu Aphunzitsa Kudzera M’mafanizo Osiyana-Siyana
Yesu Akupitiliza Kuphunzitsa Ndi Kuchilitsa Pa Ulendo Waku Yerusalemu
Yesu Aphunzitsa Ndi Mafanizo Ambiri
Yesu Aphunzitsa Za Pemphero Komanso Adzudzula Afarisi
Fanizo La Msamariya Wachifundo
Ulendo Wa Yesu Ku Yerusalemu
Yesu Aphunzitsa Kudzera M’mafanizo
Machilitso, Kuukitsa Akufa Ndi Kuyamikira Yohane M’batizi
Kusankha Ophunzira Khumi Ndi Awiri Ndi Chiphunzitso Chapachigwa
Yesu Asankha Ophunzira, Achiritsa Ndi Kuphunzitsa
Yesu Akanidwa Ndi Abale Wake
Yohane M’batizi; Kuunika Muzu WaMariya, Komanso Kuyesedwa Kwa Yesu
Simeoni Ndi Anna Azindikira Mesiya; M’nyamata Yesu Ali M’kachisi; Kuyambika Kwa Utumiki Wa Yohane
Zinthu Zomwe Zinachitika Kwa Mariya
Nyimbo Za Khisimisi
Kulengeza Kwa M’ngelo Gabrieli
Chiyambi Ndi Kuonetsa Cholinga Cha Bukhuli
Kugwiritsa Ntchito Pangano
Tsogolo La Mtundu Wa Israyeli
Chaka Chopuma Ndi Chaka Chachikondwerero
Choyikapo Nyali Ndi Mkate Woonekera
Kupitiliza Kuona Za Nyengo Yopatulika
Nyengo Kapena Nthawi Yopatulika
Kudetsedwa Kwa Unsembe Ndi Maliro
Chilango Cha Kupha
Ubale Wa Munthu
Makhalidwe Oyenera Ya Ana Amulungu
Pali Malo Amodzi Operekera Nsembe
Tsiku Lotetezera
Kuunika Zo Ukha
Mabala Akukha Kapena Mabala Otuluka Magazi
Mwambo Woyeretsa Munthu Wakhate
Kupitiliza Kuona Nkhani Ya Khate
Tikambirana Za Nthenda Ya Khate
Kutengera Uchimo Kuchokera Kwa Makolo Kapena Kuti Kupatsirana Machimo Kuchokera Kwa Makolo
Nyama Zodetsedwa Ndi Zosadetsedwa
Chakudya Cha Anthu A Mulungu
Mulungu Athana Ndi Kugalukira Ndi Kusamvera
Ntchito Ya Tsiku Ndi Tsiku Ya Ansembe
Kupatulika Kwa Ansembe
Nsembe Yopalamula Ndi Nsembe Ya Mtendere
Kuunika Za Nsembe Yopalamula
Zochimwa Za Mtundu Wonse Wa Israyeli, Mtsogoleri Ndi Anthu Wamba
Nsembe Ya Uchimo Pochimwa Wansembe
Nsembe Ya Mtendere
Nsembe Ya Ufa Ndi Ya Zipatso Zoyamba
Malamulo, Mwambo Ndi Chifukwa Chopereka Yopsereza
Chiyambi Cha Bukhu La Levitiko Ndi Za Nsembe Yopsereza